LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 9/14 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 6

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 6
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 6
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 9/14 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 6

MLUNGU WA OCTOBER 6

Nyimbo 18 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 14 ndime 14-19 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Deuteronomo 1–3 (Mph. 10)

Na. 1: Deuteronomo 2:16-30 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Tatsala Pang’ono Kupeza Mpumulo ku Zinthu Zoipa Zimene Satana Amatilimbikitsa Kucita—rs tsa. 356 ndime 3 mpaka tsa. 357 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Kuti Kugonana Konse ndi Chimo?—rs tsa. 179 ndime 1 mpaka tsa. 180 ndime 3 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 24

Mph. 10: Kugaŵila Magazini mu October. Nkhani yokambilana. Yambani ndi citsanzo coonetsa mmene tingagaŵile magazini pogwilitsila nchito maulaliki acitsanzo amene ali pa tsamba lino. Ndiyeno kambilanani mmene citsanzo ciliconse cinalili.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Mph. 10: Tinacita Zotani? Nkhani yokambilana. Pemphani ofalitsa kuti afotokoze mmene apindulila pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti, “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyala Maziko a Ulendo Wobwelelako.” Pemphani omvela kuti afotokoze zocitika zabwino za mu ulaliki.

Nyimbo 83 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani