LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/14 tsa. 3
  • Mmene Tingakhalile Acangu pa Nchito Yolalikila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mmene Tingakhalile Acangu pa Nchito Yolalikila
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Nkhani Zofanana
  • Yembekezelanibe!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Zikumbutso za Yehova Ndi Zodalilika
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 10/14 tsa. 3

LEMBA LA MWEZI: “LALIKILA MAU. LALIKILA MODZIPELEKA.”—2 Tim. 4:2.

Mmene Tingakhalile Acangu pa Nchito Yolalikila

Kuti tikapulumuke pa mapeto a dongosolo lino loipa la zinthu, tiyenela kukhala acangu pa nchito yolalikila. Tingathe kuonjezela cangu cathu mwa kutsatila zikumbutso zotsatilazi:

  • Tiyenela kupemphela nthawi zonse kuti Ufumu wa Mulungu ubwele.—Mat. 6:10.

  • Tiyenela kuteteza mtima wathu mwa kuŵelenga Baibulo tsiku ndi tsiku.—Aheb. 3:12.

  • Tifunika kugwilitsila nchito nthawi yathu mwanzelu.—Aef. 5:15, 16; Afil. 1:10.

  • Tiyenela kukhala ndi diso “lolunjika pa cinthu cimodzi,” ndipo tisamatengeke ndi zilakolako za m’dzikoli.—Mat. 6:22, 25; 2 Tim. 4:10.

  • Tiyenela kukhala maso ndi achelu pamene maulosi a m’Baibulo akukwanilitsidwa. —Maliko 13:35-37.

Kukhala acangu kudzatilimbikitsa kudzipeleka ndi mtima wonse kuti titsilize nchito imene ikugwilidwabe.—Yoh. 4:34, 35.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani