LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/14 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 22

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 22
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 22
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 12/14 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 22

MLUNGU WA DECEMBER 22

Nyimbo 15 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 2 ndime 21 mpaka 24, bokosi pa tsa. 24 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Yoswa 9-11 (Mph. 10)

Na. 1: Yoswa 9:16-27 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Palibe Mbali ya Munthu Imene Imakhalabe ndi Moyo Munthu Akafa—rs tsa. 321 ndime 6–tsa. 322 ndime 3 (Mph. 5)

Na. 3: Cifukwa Cake Tiyenela Kukhala pa Ubwenzi Wabwino ndi Yehova Ndiponso Anthu Amene Amamukonda—lv tsa. 26 ndi 27 ndime 4-7, bokosi pa tsamba 29 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: Tulutsani “zabwino” m’cuma cabwino cimene mwapatsidwa.—Mat. 12:35a.

Nyimbo 119

Mph. 5: Zosoŵa za pampingo.

Mph. 25: “Sukulu ya Ulaliki ya 2015 Idzatithandiza Kunola Luso Lathu Lophunzitsa.” Nkhani yokambilana. Ikambidwe ndi woyang’anila Sukulu ya Ulaliki. Woyang’anila sukulu angasankhe ndime zina kuti ziŵelengedwe asanayambe kukambilana ndi gulu. Fotokozani masinthidwe okhudza nkhani Na.1, nthawi ya mfundo zazikulu, ndi malangizo amene woyang’anila sukulu amapeleka. Ŵelengani ndime 7, ndiyeno pambuyo pokambilana ndimeyo, citani citsanzo coonetsa mkulu akutsogoza phunzilo la banja ndipo ali ndi mkazi wake ndi mwana wake. Pocita phunzilo limeneli, mkuluyo agwilitsile nchito nkhani imene ili pa tsamba 14 m’kabuku kakuti, Mfundo za m’Mau a Mulungu. Limbikitsani onse kuti adzapindule mokwanila ndi maphunzilo abwino a m’sukulu imeneyi ndi kugwilitsila nchito bwino buku la Pindulani ndi sukulu ya utumiki wa Mulungu.

Nyimbo 117 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani