LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/15 tsa. 4
  • Muzilimbikitsana pa Nchito Zabwino Modzipeleka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muzilimbikitsana pa Nchito Zabwino Modzipeleka
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Ganizilanani Ndi Kulimbikitsana
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Muzilimbikitsidwa ndi Mphatso ya Mulungu Yosatheka Kuifotokoza
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 2/15 tsa. 4

Muzilimbikitsana pa Nchito Zabwino Modzipeleka

Lemba la Aheberi 10:24 limatilimbikitsa kuti, “tiyeni tiganizilane kuti tilimbikitsane pa cikondi ndi nchito zabwino.” Tingalimbikitse abale athu mwa kukhala citsanzo cabwino ndi kulankhula mau oonetsa kuti tili ndi cikhulupililo. Fotokozelani ena mumpingo zocitika zabwino zimene mwakumana nazo mu ulaliki. Iwo afunika kuona kuti mukusangalala potumikila Yehova. Pa nthawi imodzimodziyo, pewani kuwayelekezela mosayenela ndi inu kapena anthu ena. (Agal. 6:4) Yesetsani kupeza njila yolimbikitsila ena pa “cikondi ndi nchito zabwino” osati pa kudziimba mlandu ndi nchito zabwino. (Onani buku la Sukulu ya Utumiki tsa. 158 ndime 4.) Ngati timalimbikitsa cikondi, ndiye kuti tidzatha kucitila ena zabwino mwakuthupi ndiponso polalikila.—2 Akor. 1:24.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani