LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 16

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 16
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 16
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 3/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa March 16

MLUNGU WA MARCH 16

Nyimbo 65 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 6 ndime 16-21, bokosi pa tsa. 65 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Samueli 5–9 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Samueli 6:10-21 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Ataliya—Mutu: Pewani Mzimu Woipa Monga wa Yezebeli—w09 4/1 tsa. 24, 25 (Mph. 5)

Na. 3: Maulosi Amene Anakwanilitsidwa pa Yesu Monga Mesiya—igw-CIN tsa. 11 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: ‘Khalani Okonzeka Kugwila Nchito Iliyonse Yabwino.’—Tito 3:1.

Nyimbo 98

Mph. 10: Anadzipeleka Mofunitsitsa—Ku Taiwan. Kukambilana kozikidwa pa Nsanja ya Mlonda ya October 15, 2014 tsamba 3 mpaka 6. Kodi ofalitsa amene achulidwa m’nkhaniyi anakonzekela bwanji kupita ku dziko lina? Nanga apeza madalitso otani?

Mph. 20: “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kupeza Anthu Owapelekela Magazini. Kukambilana. Mukamaliza kukambilana citani citsanzo cacidule coonetsa wofalitsa akuyambitsa phunzilo la Baibulo kwa munthu amene amamupelekela magazini. Ndiyeno funsani wofalitsa amene amapeleka magazini kwa munthu wina. Ndi anthu angati amene amapelekela magazini? Kodi amakonzekela bwanji ulendo ulionse? M’pempheni kuti afotokoze zocitika zosangalatsa.

Nyimbo 101 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani