LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/15 tsa. 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 6

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 6
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA APRIL 6
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 3/15 tsa. 8

Ndandanda ya Mlungu wa April 6

MLUNGU WA APRIL 6

Nyimbo 124 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo

cl mutu 7 ndime18-22, bokosi pa tsa. 75 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Samueli 16-18 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Samueli 18:17-24 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Mulungu Ndiye Amacititsa Kuti Anthu Azivutika?—igw-CIN tsa.14 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Baraki—Mutu: Khalani Olimba Mtima Ndipo Musadzipezele Ulemelelo—w12 2/15 tsa. 12 ndime 9 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: ‘Khalani Okonzeka Kugwila Nchito Iliyonse Yabwino.’—Tito 3:1.

Nyimbo 85

Mph. 10: Kugaŵila Magazini mu April. Kukambilana. Yambani ndi citsanzo coonetsa mmene tingagaŵile magazini pogwilitsila nchito maulaliki acitsanzo. Kenako kambilanani maulaliki onse a citsanzo.

Mph. 10: Tinacita Zotani? Kukambilana. Pemphani omvela kuti akambe mapindu amene apeza pogwilitsila nchito mfundo za m’nkhani yakuti, “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kupeza Anthu Owapelekela Magazini.” Ndiyeno afotokoze zocitika zabwino za mu ulaliki.

Mph. 10: Zosoŵa za pampingo.

Nyimbo 106 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani