LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 9/15 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 21

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 21
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA SEPTEMBER 21
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 9/15 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa September 21

MLUNGU WA SEPTEMBER 21

Nyimbo 53 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 15 ndime 20-23 ndi bokosi pa tsa. 157 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 2 Mafumu 19-22 (Mph. 8)

Na. 1: 2 Mafumu 20:12-21 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Ehudi—Mutu: Yehova Amapulumutsa Anthu Ake (w04 3/15 tsa. 29-31) (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mau Akuti “Ame” Amatanthauza Ciani? (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Kucitila umboni mokwanila za uthenga wabwino.”—Machitidwe 20:24.

Nyimbo 97

Mph. 10: Kodi Tinacita Zotani Caka Catha? Nkhani yokambidwa ndi woyang’anila nchito. Fotokozani zimene mpingo unacita caka catha. Chulani zinthu zabwino zimene mpingo unacita ndipo uyamikileni pa zimenezo. Fotokozani mfundo imodzi kapena ziŵili zimene mpingo uyenela kuongolela caka cino ndipo fotokozani mmene ungacitile zimenezo.

Mph. 10: Kucitila Umboni Mokwanila Kumabala Zipatso. Kukambilana kozikidwa pa Buku Lapacaka la 2015, tsa. 54, ndime 1; tsa. 56, ndime 2, mpaka tsa. 57, ndime 1; ndi tsa. 63, ndime 2 mpaka 64, ndime 1. Mukakambilana citsanzo ciliconse, pemphani omvela kuti akambe zimene aphunzilapo.

Mph. 10: “Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 81 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani