LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 July tsa. 4
  • Kodi Mungayeseko kwa Caka Cimodzi?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mungayeseko kwa Caka Cimodzi?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Upainiya Umalimbitsa Unansi Wathu Ndi Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • “Paulo Anayamika Mulungu Ndipo Analimba Mtima”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 July tsa. 4

UMOYO WATHU WACIKHIRISTU

Kodi Mungayeseko kwa Caka Cimodzi?

Abale aŵili aŵelengela munthu lemba mu ulaliki wa khomo ndi khomo

Kuyesako ciani? Upainiya wa nthawi zonse. Mudzapeza madalitso ambili mukakhala mpainiya—Miy. 10:22.

KUKHALA MPAINIYA KUDZAKUTHANDIZANI . . .

  • kukulitsa luso lolalikila, ndipo mudzasangalala kwambili ndi utumiki wanu

  • kulimbitsa ubwenzi wanu ndi Yehova. Mukamauza ena za iye, mudzayamba kuganizila kwambili makhalidwe ocititsa cidwi a Mulungu

  • kukhala wokhutila cifukwa coika Ufumu patsogolo mu umoyo wanu. Ndipo mudzakhala ndi cimwemwe kaamba ka kudzipeleka kuti muthandize ena. —Mat. 6:33; Mac. 20:35

  • kukhala ndi mwayi wopezeka pa miting’i ya apainiya pamene woyang’anila dela akucezela mpingo wanu, miting’i yapadela msonkhano wadela usanayambe, ndi kupezeka pa Sukulu ya Apainiya

  • kukhala ndi mwayi woyambitsa ndi kutsogoza maphunzilo ambili a Baibulo

  • kukhala ndi nthawi yambili yoceza ndi kulimbikitsana ndi alaliki anzanu. —Aroma 1:11, 12

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani