LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsa. 3
  • “Mfumu Idzalamulila Mwacilungamo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mfumu Idzalamulila Mwacilungamo”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • “Mukhale Chelu ndi Kuyang’anila Gulu Lonse la Nkhosa”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Abusa, Tsanzilani Abusa Aakulu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 January tsa. 3

CUMA COCOKELA M’MAU A MULUNGU | YESAYA 29-33

“Mfumu Idzalamulila Mwacilungamo”

Mfumu Yesu, waika “akalonga,” amene ni akulu, kuti asamalile nkhosa

32:1-3

  • Mofanana ndi “malo ousapo mvula yamkuntho,” akulu amateteza nkhosa ku mazunzo na zinthu zolefula

  • Mofanana ndi “mitsinje yamadzi m’dziko lopanda madzi,” akulu amatsitsimula amene ali na ludzu lauzimu, mwa kuwapatsa coonadi coyela, cosasukuluka

  • Mofanana ndi “mthunzi wa thanthwe lalikulu m’dziko louma,” akulu amateteza nkhosa mwa kuzipatsa malangizo ndi kuzitsitsimula

    M’nthawi za m’Baibo, munthu amatha kubisala mvula yacimphepo, kumwa madzi mu mtsinje, ndi kupumula mu mthunzi wa thanthwe
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani