LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsa. 7
  • January 30–February 5

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • January 30–February 5
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 January tsa. 7

January 30–February 5

YESAYA 43-46

  • Nyimbo 33 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Maulosi Onse a Yehova Amakwanilitsika”: (10 min.)

    • Yes. 44:26-28—Yehova anakambilatu kuti Yerusalemu na kacisi adzamangiwanso, ndipo anati Koresi ni amene adzagonjetsa Babulo (ip-2 71-72 pala. 22-23)

    • Yes. 45:1, 2—Yehova anafotokozelatu mmene mzinda wa Babulo udzagonjetsedwela (ip-2 77-78 pala. 4-6)

    • Yes. 45:3-6—Yehova anakamba zifukwa zimene anaseŵenzetsela Koresi kugonjetsa Babulo (ip- 2 79-80 pala. 8-10)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yes. 43:10-12—Kodi Aisiraeli anakhala bwanji mtundu wa mboni za Yehova? (w14 11/15 peji 21-22 pala. 14-16)

    • Yes. 43:25, Buku lopatulika—Kodi cifukwa cikulu cimene Yehova amafafanizila zolakwa zathu n’ciani? (ip-2 peji 60 pala. 24)

    • Kodi ine pacanga, kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno kwaniphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno zimene ine pacanga ningaseŵenzetse mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. kapena zocepelapo) Yes. 46:1-13

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 min. kapena zocepelapo) fg—Citani ulaliki wamwamwai kwa mnzanu wa kusukulu kapena wa kunchito.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 min. kapena zocepelapo) fg—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. kapena zocepelapo) jl phunzilo 4

UMOYO WATHU WACIKHIRISTU

  • Nyimbo 143

  • Tingatsimikizile Bwanji Kuti Baibulo Limakamba Zoona?: (15 min.) Tambitsani Vidiyo imeneyi yakuti Tingatsimikizile Bwanji Kuti Baibulo Limakamba Zoona? (Yendani ku mavidiyo pa MISONKHANO NA UTUMIKI WATHU). Ndiyeno kambilanani mafunso aya: Kodi vidiyo imeneyi tingaiseŵenzetse bwanji polalikila mwamwai, pa ulaliki wapoyela, kapena polalikila ku nyumba na nyumba? Tisimbilen’koni zabwino zimene zinacitika potambitsa vidiyoyi mu ulaliki?

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 7 pala. 19-23, bokosi papeji 75, na chati papeji 76-77, na bokosi lobwelelamo papeji 77

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Mlungu Wotsatila (3 min)

  • Nyimbo 103 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani