LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsa. 6
  • Kodi Mudzaikidwa Cizindikilo Kuti Mudzapulumuke?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mudzaikidwa Cizindikilo Kuti Mudzapulumuke?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 June tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EZEKIELI 6-10

Kodi Mudzaikidwa Cizindikilo Kuti Mudzapulumuke?

Masomphenya a Ezekieli anakwanilitsika koyamba pakuonongedwa kwa Yerusalemu. Nanga masiku ano akukwanilitsika bwanji?

9:1, 2

  • Munthu amene ananyamula kacikwama ka mlembi aimila Yesu Khristu

  • Amuna 6 amene ananyamula zida zoonongela aimila asilikali a kumwamba, ndipo Khristu ndiye mtsogoleli wawo

Munthu adindidwa cizindikilo pa mphumi; Amuna 6 anyamula zida zoonongela

9:3-7

  • Akhamu lalikulu adzaikiwa cizindikilo pamene adzaweluzidwa kuti ni nkhosa mkati mwa cisautso cacikulu

Yesu alamula angelo

Niyenela kucita ciani kuti nidzaikidwe cizindikilo codzapulumuka?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani