LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsa. 4
  • Khalani m’Cigwa ca “Pakati pa Mapili”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani m’Cigwa ca “Pakati pa Mapili”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 December tsa. 4
Anthu akuyenda m’cigwa ca “pakati pa mapili”

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | ZEKARIYA 9-14

Khalani m’Cigwa ca “Pakati pa Mapili”

14:3-5

Yehova anapanga “cigwa cacikulu kwambili” mu 1914, pamene anakhazikitsa Ufumu wa Mesiya, umene ni “phili” locepelapo pa ulamulilo wake wa cilengedwe conse. Kuyambila mu 1919, atumiki a Mulungu akhala otetezeka m’cigwa ca “pakati pa mapili” cimeneco

Kodi anthu amathaŵila motani ku cigwa ca citetezo?

14:12, 15

Aliyense amene adzakhala kunja kwa cigwa cophiphilitsaco adzawonongedwa pa Aramagedo

Ningacite ciani kuti nikhale m’cigwa ca citetezo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani