LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsa. 6
  • MpingoWacikhristu Watsopano Uyesedwa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • MpingoWacikhristu Watsopano Uyesedwa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Yehova Amafunanji kwa Ise?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Anthu Atema Miyala Stefano
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Mzimu Woyela Unatsanulidwa pa Mpingo Wacikhristu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 November tsa. 6
Sitefano akuponyedwa miyala ndipo Saulo akuona komanso akugwilizana nazo

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 6-8

MpingoWacikhristu Watsopano Uyesedwa

6:1-7; 7:58–8:1

Akazi amasiye okamba Cigiriki amene anali atangobatizika kumene, komanso amene anakhala nthawi yaitali ku Yerusalemu, anali kunyalanyazidwa. Kodi kupanda cilungamo kumeneko kunawakhumudwitsa, kapena anayembekezela pa Yehova kuti iye adzakonza zinthu?

Pambuyo pakuti Sitefano waponyewa miyala, komanso pamene cizunzo coopsa cinacititsa Akhristu a ku Yerusalemu kuthaŵila kumadela a ku Yudeya na ku Samariya, kodi iwo anazilala pa nchito yawo yolalikila?

Cifukwa ca thandizo la Yehova, mpingo watsopano umenewu unapilila ndipo unakula.—Mac. 6:7; 8:4.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimacita bwanji nikakumana na mayeselo?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani