LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsa. 3
  • Apatsidwa Mlandu Wakuti ni Wovutitsa Komanso Woukila Boma

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Apatsidwa Mlandu Wakuti ni Wovutitsa Komanso Woukila Boma
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Paulo Apempha Kukaonekela kwa Kaisara Kenako Alalikila Mfumu Herode Agiripa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 January tsa. 3
Mwana wa mlongosi wake wa Paulo akamba na mkulu wa asilikali

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 23-24

Apatsidwa Mlandu Wakuti ni Wovutitsa Komanso Woukila Boma

23:12, 16; 24:2, 5, 6, 10-21

Ayuda a ku Yerusalemu ‘analumbila mwa kudzitembelela’ n’colinga cakuti aphe Paulo. (Mac. 23:12) Komabe, colinga ca Yehova cinali cakuti Paulo apite ku Roma kukacitila umboni. (Mac. 23:11) Mwana wamwamuna wa mlongo wake wa Paulo atamva za ciwembuco, anakanena kwa Paulo, pofuna kumuteteza kuti asaphedwe. (Mac. 23:16) Kodi cocitikaci cakuphunzitsani ciani ponena za . . .

  • amene amayesa kulepheletsa colinga ca Mulungu?

  • njila imene Mulungu angaseŵenzetse potithandiza?

  • kulimba mtima?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani