LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsa. 4
  • January 21-27

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • January 21-27
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 January tsa. 4

January 21-27

MACHITIDWE 25-26

  • Nyimbo 73 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Paulo Apempha Kukaonekela kwa Kaisara Kenako Alalikila Mfumu Herode Agiripa”: (10 min.)

    • Mac. 25:11—Paulo anaseŵenzetsa ufulu wake wa lamulo kuti akaonekele kwa Kaisara (bt peji 198 pala. 6)

    • Mac. 26:1-3—Paulo mwaluso anaikila kumbuyo coonadi pa maso pa Mfumu Herode Agiripa (bt mape. 198-201 mapa. 10-16)

    • Mac. 26:28—Mfumuyo inakhudzika mtima kwambili na mawu a Paulo (bt peji 202 pala. 18)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Mac. 26:14—Kodi cisonga cotosela n’ciani? (“kuponya miyendo yake kuti imenye zisonga zotosela” nwtsty mfundo younikila; nwt matanthauzo a mawu ena, ‘cisonga cotosela’)

    • Mac. 26:27—N’cifukwa ciani Mfumu Agiripa anavutika kuyankha Paulo atamufunsa ngati anali kukhulupilila zolemba za aneneli? (03 11/15 mape. 16-17 pala. 14)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mac. 25:1-12 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Kubwelelako Koyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Kubwelelako Koyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 2)

  • Kubwelelako Koyamba: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno gaŵilani buku lakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse. (th phunzilo 3)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 38

  • “Kupatsidwa Ufulu Wolalikila ku Quebec”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 51

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 122 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani