LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsa. 4
  • Paulo Apempha Kukaonekela kwa Kaisara Kenako Alalikila Mfumu Herode Agiripa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Paulo Apempha Kukaonekela kwa Kaisara Kenako Alalikila Mfumu Herode Agiripa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Apatsidwa Mlandu Wakuti ni Wovutitsa Komanso Woukila Boma
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 January tsa. 4
Paulo waima pamaso pa Mfumu Herode Agiripa, ndipo akumulalikila

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 25-26

Paulo Apempha Kukaonekela kwa Kaisara Kenako Alalikila Mfumu Herode Agiripa

25:11; 26:1-3, 28

Ngakhale kuti sitifunika kuda nkhawa kuti tidzakamba ciani akatipeleka kwa “abwanamkubwa ndi mafumu,” tifunika ‘kukhala okonzeka nthawi zonse kuyankha’ aliyense amene watifunsa za ciyembekezo cathu. (Mat. 10:18-20; 1 Pet. 3:15) Tingatengele bwanji citsanzo ca Paulo ngati otsutsa “akuyambitsa mavuto mwa kupanga malamulo”?—Sal. 94:20.

  • Mwa kuseŵenzetsa ufulu wathu wa lamulo poteteza uthenga wabwino.—Mac. 25:11

  • Mwa kukhala aulemu pokamba na akulu-akulu a boma.—Mac. 26:2, 3

  • Ngati m’poyenela, mwa kufotokoza mmene uthenga wabwino watipindulitsila na mmene wapindulitsila ena.—Mac. 26:11-20

Mlongo waima pamaso pa woweluza ndipo akumulalikila

Kodi munaganizapo mmene mungayankhile ngati ena akufunsani zimene mumakhulupilila?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani