LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsa. 5
  • Kupatsidwa Ufulu Wolalikila ku Quebec

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kupatsidwa Ufulu Wolalikila ku Quebec
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • N’napeza Madalitso Ambili Cifukwa Cophunzila kwa Ofalitsa Acitsanzo Cabwino
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Alaliki a Ufumu Amapeleka Milandu Yao ku Khoti
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 January tsa. 5

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kupatsidwa Ufulu Wolalikila ku Quebec

Kaisara, msilikali waciroma, na Paulo

Pa nthawi imene Paulo anali kuimbidwa mlandu, anapempha kuti akaonekele kwa Kaisara. Poseŵenzetsa ufulu wake monga nzika ya Roma, iye anatipatsa citsanzo cabwino cofunika kutengela masiku ano. Tambitsani vidiyo yakuti “Kupatsidwa Ufulu Wolalikila ku Quebec,” kuti tidziŵe mmene abale anaseŵenzetsela ufulu wa lamulo poteteza uthenga wabwino ku Quebec. Pambuyo pake, yankhani mafunso aya:

Mboni za Yehova ku Quebec m’ma 1940; kathilakiti kapadela; m’bale akukamba nkhani mu ulaliki pa nthawi ya ciletso; M’bale Aimé Boucher
  • Kodi abale athu ku Quebec anakumana na mavuto otani?

  • Ni kathirakiti kati kapadela kamene iwo anagaŵila? Nanga panakhala zotulukapo zanji?

  • N’ciani cinacitikila M’bale Aimé Boucher?

  • Kodi Khoti Lalikulu ku Canada linagamula ciani pa mlandu wa M’bale Boucher?

  • Ni ufulu wa lamulo uti umene suseŵenza kaŵili-kaŵili umene abalewa anauseŵenzetsa? Nanga panakhala zotulukapo zabwanji?

  • N’ciani cinacitika pambuyo pakuti apolisi motunthiwa na ansembe aimitsa misonkhano yampingo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani