LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 February tsa. 2
  • Pitilizani Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitilizani Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Mmene Mungasungile Cikumbumtima Cabwino
    “Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu”
  • Khalani Na Cikumbumtima Cabwino Kwa Mulungu
    Mmene Tingakhalilebe mu Cikondi ca Mulungu
  • Lolani Malamulo a Mulungu na Mfundo Zake Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Kodi Muli na Mtima wa Mnofu?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 February tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 1-3

Pitilizani Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu

M’bale akusinkha-sinkha pambuyo pocita phunzilo la umwini

2:14, 15

Cikumbumtima cathu cingatithandize ngati

  1. ticiphunzitsa mfundo za m’Baibo

  2. ticimvelela cikatikumbutsa mfundo zimenezo

  3. tipempha mzimu woyela kuti utithandize kusacita zoipa.—Aroma 9:1

Ni mfundo ziti zimene ningafunike kuganizila . . .

  • Mwamuna na mkazi wake akukana kumwa moŵa

    ngati nifuna kusankha kumwa kapena kusamwa mowa?

  • Mlongo wacicepele akusankha siketi

    posankha zovala komanso podzikongoletsa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani