LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsa. 8
  • Kodi Mungaphunzile Ciani kwa Iwo?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mungaphunzile Ciani kwa Iwo?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Lemekezani Ena
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
  • N’cifukwa Ciyani Ulemu Ni Wofunika?
    Galamuka!—2024
  • Inu Abale Acinyamata​—Khalani Amuna Okhwima Mwauzimu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Atumiki Othandiza Amacita Utumiki Wofunika
    Gulu Lokhazikitsidwa Kucita Cifunilo ca Yehova
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 July tsa. 8
Elisa apenyelela pamene Eliya akupatutsa madzi na covala cake mu mtsinje wa Yorodano

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kodi Mungaphunzile Ciani kwa Iwo?

Kodi ndinu mkulu kapena mtumiki wothandiza watsopano? N’kutheka kuti muli na maluso, mphatso, kapena munapata maphunzilo a kuthupi kuposa akulu na atumiki othandiza ena mu mpingo mwanu. Ngakhale n’conco, pali zambili zimene mungaphunzile kwa abale amene ali m’bungwe la atumiki. Mungaphunzilenso zambili kwa amuna okhulupilika amene satumikilanso m’bungweli cifukwa ca zovuta zina monga ukalamba, thanzi, kapena cifukwa ca maudindo a m’banja.

TAMBITSANI VIDIYO YAKUTI MUZILEMEKEZA ACIYAMBAKALE, PAMBUYO PAKE YANKHANI MAFUNSO AYA:

  1. M’bale Richards aŵelengela lemba m’bale Ben

    1. Kodi M’bale Richards anaonetsa bwanji kuti amalemekeza M’bale Bello?

  2. Ben aseŵenzela pa mapu ya magawo

    2. Kodi m’bale Ben analakwitsa ciani? Nanga n’cifukwa ciani?

  3. M’bale Bello akambilana na Ben pamene alandila cakudya pamodzi

    3. Kodi Ben anaphunzilapo ciani pa citsanzo ca Elisa?

  4. 4. Kaya ndinu m’bale kapena mlongo, kodi mungaonetse bwanji kuti mumalemekeza Akhristu amene ni aciyambakale? Nanga mungacite ciani kuti muphunzile kwa iwo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani