LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsa. 2
  • September 2-8

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 2-8
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 September tsa. 2

September 2-8

AHEBERI 7-8

  • Nyimbo 16 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Wansembe Mpaka Muyaya Monga mwa Unsembe wa Melekizedeki”: (10 min.)

    • Aheb. 7:1, 2—Melekizedeki, Mfumu komanso Wansembe, anakumana na Abulahamu na kumudalitsa (it-2 366)

    • Aheb. 7:3—Melekizedeki “analibe mzele wa mibadwo ya makolo” komanso “iye ndi wansembe kwamuyaya” (it-2 367 ¶4)

    • Aheb. 7:17—Yesu ni “wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melekizedeki” (it-2 366)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Aheb. 8:3—Kodi pali kusiyana kwanji pakati pa mphatso na nsembe zimene zinali kupelekedwa m’Cilamulo ca Mose? (w00 8/15 14 ¶11)

    • Aheb. 8:13—Kodi pangano la Cilamulo linaleka bwanji kugwila “nchito” m’nthawi ya Yeremiya? (it-1 523 ¶5)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Aheb. 7:1-17 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Kuseŵenzetsa Bwino Zitsanzo Zooneka, ndiyeno kambilanani phunzilo 9 m’bulosha ya Kuphunzitsa.

  • Nkhani: (5 min. olo kucepelapo) it-1 524 ¶3-5​—Mutu: Kodi cipangano catsopano n’ciani? (th phunzilo 7)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 124

  • Zimene Gulu Likukwanilitsa: (15 min.) Tambitsani vidiyo ya Zimene Gulu Likukwanilitsa ya September. Limbikitsani onse kukaonako likulu lathu kapena nthambi ya m’dziko lawo ngati n’kotheka.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 82

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 83 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani