LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsa. 4
  • Zotulukapo Zoipa za Bodza Loyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zotulukapo Zoipa za Bodza Loyamba
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • “Dzina Lanu Liyeletsedwe”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Tizikamba Zoona
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Kodi Mulungu Ali Nalo Colinga Canji Dziko Lapansi?
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
  • N’cifukwa Ciani Mulungu Amalolela Kuti Anthu Azivutika?
    Uthenga Wabwino Wocokela kwa Mulungu
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 January tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 3-5

Zotulukapo Zoipa za Bodza Loyamba

3:1-6, 15-19

Zithunzi: 1. Satana akuseŵenzetsa cinjoka pokamba na Hava. 2. Adamu na Hava akalamba ndipo ali na thanzi lofooka. 3. Mzela wa anthu kucoka pa Adamu na Hava mpaka masiku ano, kuimila nthawi zosiyana-siyana, mitundu, na zikhalidwe.

Satana wakhala akusoceletsa anthu kucokela pamene ananamiza Hava. (Chiv. 12:9) Kodi mabodza otsatilawa amene Satana amacilikiza atsekeleza bwanji anthu kuyandikila Yehova?

  • Kulibe Mulungu wamphamvuzonse

  • Mulungu ni Utatu Wosamvetsetseka

  • Mulungu alibe dzina

  • Mulungu amalanga anthu m’moto wa helo kwamuyaya

  • Zonse zimene zimacitika n’cifunilo ca Mulungu

  • Mulungu sasamala za anthu

Kodi mumamvela bwanji mukaganizila mabodza onyoza Mulungu amenewa?

Kodi mungathandizile bwanji pa kuyeletsa dzina la Mulungu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani