LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 April tsa. 1
  • Makambilano Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Makambilano Acitsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWELELAKO WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWELELAKO WACIŴILI
  • KAMPENI YOMEMEZA ANTHU KU CIKUMBUTSO (March 14–April 7):
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 April tsa. 1
Yesu akudya Pasika ndi atumwi ake okhulupilika.

Yesu acita cipangano na atumwi ake okhulupilika

Makambilano Acitsanzo

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi cifunilo ca Mulungu kwa anthu n’ciani?

Lemba: Gen. 1:28

Ulalo: Tidziŵa bwanji kuti Mulungu adzakwanilitsa cifunilo cake kwa anthu?

PEZANI LEMBALI M’CIDA CA M’THUBOKSI YATHU:

  • Buku yakuti ‘Zimene Baibulo Ingatiphunzitse’

    bhs 29 ¶1

○●○ ULENDO WOBWELELAKO WOYAMBA

Funso: Tidziŵa bwanji kuti Mulungu adzakwanilitsa cifunilo cake kwa anthu?

Lemba: Yes. 55:11

Ulalo: Kodi umoyo udzakhala bwanji Mulungu akadzakwanilitsa cifunilo cake?

PEZANI LEMBALI M’CIDA CA M’THUBOKSI YATHU:

  • Buku yakuti ‘Zimene Baibulo Ingatiphunzitse’

    bhs 29 ¶2

○○● ULENDO WOBWELELAKO WACIŴILI

Funso: Kodi umoyo udzakhala bwanji Mulungu akadzakwanilitsa cifunilo cake?

Lemba: Sal. 37:10, 11

Ulalo: Kodi tifunika kucita ciani kuti tikapindule na malonjezo a Mulungu?

PEZANI LEMBALI M’CIDA CA M’THUBOKSI YATHU:

  • Buku yakuti ‘Zimene Baibulo Ingatiphunzitse’

    bhs 35 ¶17

KAMPENI YOMEMEZA ANTHU KU CIKUMBUTSO (March 14–April 7):

“Tabwela kudzakuitanilani ku cocitika capadela ca anthu mamiliyoni ambili. Cocitika cimeneci ni mwambo wokumbukila imfa ya Yesu.” Ndiyeno patsani munthuyo kapepa ka ciitanilo. “Kapepa ka ciitanilo aka kaonetsa nthawi na malo kumene cocitikaci cidzacitikile kwathu kuno. Tikuitanilaninso ku nkhani yapadela imene idzakambidwa pa wikendi yoti cikumbutso cicitika wiki yotsatila.”

Funso la Ulalo Akaonetsa Cidwi: N’cifukwa ciani Yesu anafa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani