LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 April tsa. 6
  • Zotulukapo Zoopsa za Mayanjano Oipa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zotulukapo Zoopsa za Mayanjano Oipa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Muziyanjana na Anthu Okonda Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Kondani Anthu Amene Mulungu Amakonda
    “Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu”
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • Kodi Yehova Amafunanji kwa Ise?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 April tsa. 6
M’bale akumwa mowa na anzake ogwila naye nchito pambuyo pokomboka ku nchito. Iye akumvetsela mowadela nkhawa pamene akukambilana zinthu zimene amakonda, monga zovala, magemu, ndalama, komanso zipangizo zamakono.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 34-35

Zotulukapo Zoopsa za Mayanjano Oipa

34:1, 2, 7, 25

Ngati maneba athu, anzathu a kunchito kapena a kusukulu ali na makhalidwe abwino, kodi zitanthauza kuti angakhale mabwenzi abwino? N’ciani cingatithandize kudziŵa ngati munthu wina ni bwenzi labwino kapena ayi?

  • Kodi kukhala nawo paubwenzi kudzanithandiza kulimbitsa ubale wanga na Yehova?

  • Kodi zokamba zawo zimaonetsa kuti cofunika kwambili kwa iwo n’ciani?—Mat. 12:34

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi mabwenzi anga amanilimbikitsa kukhala pa ubale wabwino na Yehova?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani