LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsa. 6
  • Yosefe Anacita Zinthu Modziletsa Kwambili

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yosefe Anacita Zinthu Modziletsa Kwambili
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Tamvelani Maloto Awa’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Abale Ake Amuzonda Yosefe
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Yehova Sanamuiŵale Yosefe
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Kapolo Amene Anamvela Mulungu
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 May tsa. 6
Yosefe alila pamene abale ake aimilila ca kumbuyo.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 42-43

Yosefe Anacita Zinthu Modziletsa Kwambili

42:5-7, 14-17, 21, 22

Ganizilani cabe mmene Yosefe anamvelela pamene anaonana na abale ake pamaso m’pamaso mosayembekezela. Mwamsanga akanafuna kudziulula, ndipo akanawakumbatila, kapena akanasankha kubwezela pa zimene iwo anamucitila. Koma iye sanacite zinthu mopupuluma. Kodi mungacite ciani ngati a m’banja lanu kapena anthu ena akukucitilani zinthu zopanda cilungamo? Citsanzo ca Yosefe citiphunzitsa kuti kucita zinthu modziletsa n’kofunika. Citiphunzitsanso kuti tifunika kukhala wodekha m’malo motsatila mtima wathu wonyenga kapena kucita zinthu mogwilizana na mmene timvelela mu mtima.

Kodi mungatengele bwanji citsanzo ca Yosefe pa zocitika zosiyana-siyana zimene mumakumana nazo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani