LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsa. 6
  • July 27–August 2, 2020

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 27–August 2, 2020
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 July tsa. 6

July 27–August 2

EKSODO 12

  • Nyimbo 20 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mwambo wa Pasika—Zimene Umatanthauza kwa Akhristu”: (10 min.)

    • Eks. 12:5-7—Zimene mwana wa nkhosa wocitila Pasika anali kuimila (w07 1/1 20 ¶4)

    • Eks. 12:12, 13—Zimene kuwaza magazi pa khomo kunali kutanthauza (it-2 583 ¶6)

    • Eks. 12:24-27—Zimene tiphunzilapo pa mwambo wa Pasika (w13 12/15 20 ¶13-14)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Eks. 12:12—Kodi ni motani mmene milili kwa Aiguputo, maka-maka wa namba 10, unali ciweluzo kwa milungu yawo yonama? (it-2 582 ¶2)

    • Eks. 12:14-16—N’ciani cinali capadela na Cikondwelelo ca Mikate Yopanda Cofufumitsa komanso misonkhano ina yopatulika? Nanga inali kuŵapindulitsa motani Aisiraeli? (it-1 504 ¶1)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Eks. 12:1-20 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso, kopani cidwi cake. (th phunzilo 2)

  • Ulendo Wobwelelako: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo, ndiyeno gaŵilani magazini yaposacedwa yogwilizana na nkhani imene mwakambilana. (th phunzilo 6)

  • Phunzilo la Baibo: (5 min. olo kucepelapo) bhs 16 ¶21-22 (th phunzilo 19)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 38

  • “Yehova Amateteza Anthu Ake”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Kuyendela Miziyamu ya ku Warwick: “Anthu Odziŵika na Dzina la Yehova”.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 125

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 129 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani