LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsa. 1
  • Makambilano Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Makambilano Acitsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • ●○ ULENDO WOYAMBA
  • ○● ULENDO WOBWELELAKO
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Makambilano Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 July tsa. 1
Mose na Aroni acita zozizwitsa pamaso pa Farao na anthu ake ogwila nchito m’nyumba yacifumu. Ndodo ya Aroni ikusanduka njoka.

Mose na Aroni acita zozizwitsa pamaso pa Farao

Makambilano Acitsanzo

●○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Tidziŵa bwanji kuti mavuto amene timakumana nawo si cilango cocokela kwa Mulungu?

Lemba: Yak. 1:13

Ulalo: N’cifukwa ciani timavutika?

PEZANI LEMBALI M’CIDA CA M’THUBOKSI YATHU:

  • Buku la ‘Zimene Baibulo Ingatiphunzitse’

    bhs 9 ¶7

○● ULENDO WOBWELELAKO

Funso: N’cifukwa ciani timavutika?

Lemba: 1 Yoh. 5:19

Ulalo: Kodi Mulungu amamvela bwanji akaona kuti tikuvutika?

PEZANI LEMBALI M’CIDA CA M’THUBOKSI YATHU:

  • Buku la ‘Zimene Baibulo Ingatiphunzitse’

    bhs 117 ¶7

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani