LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 1
  • Makhalidwe a Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Makhalidwe a Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Makhalidwe a Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Pemphelo la Mtumiki wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 1

Nyimbo 1

Makhalidwe a Yehova

(Chivumbulutso 4:11)

1. Yehova Mulungu, wamphamvu,

Mwini moyo komanso kuwala.

Mphamvu zanu zimaonekera

M’zinthu zomwe munalenga.

2. Ndinu Mfumu ya chilungamo,

Mumatiphunzitsa malamulo.

Tikamaphunzira Mawu anu,

Timaona nzeru zanu.

3. Chikondi chanu ndi changwiro.

Sitingathe kukubwezerani.

Makhalidwe anu n’ngapamwamba,

Tidzalengeza mokondwa.

(Onaninso Sal. 36:9; 145:6-13; Yak. 1:17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani