LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 1
  • Makhalidwe a Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Makhalidwe a Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Makhalidwe a Yehova
    Imbirani Yehova
  • Yehova​—Amatisamalila ndi Kutiteteza
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Pemphelo la Mtumiki wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mulungu Ali na Makhalidwe Abwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2019
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 1

NYIMBO 1

Makhalidwe a Yehova

Yopulinta

(Chivumbulutso 4:11)

  1. 1. Mulungu wathu wamphamvu zonse.

    Tiyamikila potipatsa moyo.

    Cilengedwe canu cimanena

    za mphamvu zanu zodabwitsa.

  2. 2. Yehova ndimwe wokoma mtima.

    Ufumu wanu ni wacilungamo.

    Mau anu amapatsa nzelu.

    Timalengeza njila zanu.

  3. 3. Mumatipatsa zonse zabwino.

    Cikondi canu cimatidabwitsa.

    Mwa cimwemwe tikuimbilani.

    Tidzatamanda dzina lanu.

(Onaninso Sal. 36:9; 145:6-13; Mla. 3:14; Yak. 1:17)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani