LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 17
  • Pitani Patsogolo Mboninu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitani Patsogolo Mboninu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Patsogolo! Inu Mboni Zake
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Dzina Lanu Ndimwe Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 17

Nyimbo 17

Pitani Patsogolo Mboninu!

(Luka 16:16)

1. Olimba m’nthawi yamapeto ino,

Ndife oteteza uthenga wabwino.

Satana ’ngatsutse koopsa,

Mumphamvu ya Mulungu sitigonja.

(KOLASI)

Ndiye pitani patsogolo Mboninu!

Kondwerani pogwira ntchito ya M’lungu!

Uzani onse zadziko latsopano

Momwe mudzakhala madalitso.

2. Tisatengeke ndi moyo wofewa,

Kusangalatsa dzikoli tizipewa.

Mawanga a dziko tikane

Ndi kukhala okhulupirikabe.

(KOLASI)

Ndiye pitani patsogolo Mboninu!

Kondwerani pogwira ntchito ya M’lungu!

Uzani onse zadziko latsopano

Momwe mudzakhala madalitso.

3. Ufumu wa M’lungu ukunyozedwa,

Dzina lake loyera likudetsedwa.

Tiyenitu tiliyeretse,

Kumitundu yonse tililengeze.

(KOLASI)

Ndiye pitani patsogolo Mboninu!

Kondwerani pogwira ntchito ya M’lungu!

Uzani onse zadziko latsopano

Momwe mudzakhala madalitso.

(Onaninso Afil. 1:7; 2 Tim. 2:3, 4; Yak. 1:27.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani