LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 97
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Patsogolo! Inu Mboni Zake
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
  • “Lalikila Mau”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 97

Nyimbo 97

Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!

(2 Timoteyo 4:5)

1. Pitani patsogolo ndithu

Polalikira konse.

Muthandize anthu ofatsa

Cho’nadi achikonde.

Ndi mwayidi kutumikira,

Tikonda kulalikira.

Chitirani umboni M’lungu

Ndi dzina lake loyera.

(KOLASI)

Pitirizani kulalikira

padziko lonse.

Pitirizani kukhala

okhulupirikabe.

2. Atumiki enieninu

Pitani patsogolo.

Timatsatira Mbuye wathu.

Tidzalandira mphoto.

Ndi kofunika kuti anthu

Amve uthenga wa M’lungu.

Yehova atipatsa mphamvu

Ndipo sitiopa kanthu!

(KOLASI)

Pitirizani kulalikira

padziko lonse.

Pitirizani kukhala

okhulupirikabe.

3. Tipite patsogolo tonse,

Amuna ndi akazi.

Otsalira ndi nkhosa zina

Tiziyenda m’cho’nadi.

Wathu si utumiki wamba.

Kwa ife n’ngopatulika.

Tiyeni tisonyeze M’lungu

Kuti ndife oyenera.

(KOLASI)

Pitirizani kulalikira

padziko lonse.

Pitirizani kukhala

okhulupirikabe.

(Onaninso Sal. 23:4; Mac. 4:29, 31; 1 Pet. 2:21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani