LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 19
  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mulungu Watilonjeza Paradaiso
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Analonjeza Paradaiso
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Tidzaonana M’Paradaiso!”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 19

Nyimbo 19

Mulungu Watilonjeza Paradaiso

(Luka 23:43)

1. M’lungu wathu watilonjeza

Paradaiso wam’tsogolo.

Adzachotsa uchimo, imfa,

Zopweteka ndi misozi.

(KOLASI)

Paradaiso adzafika.

Ndipo sitikukayika.

Khristu adzakwaniritsa

Chifuniro cha Mulungu.

2. Cholinga cha Mulungu n’choti

Yesu aukitse anthu.

Monga Yesu analonjeza,

‘Udzakhala m’Paradaiso.’

(KOLASI)

Paradaiso adzafika.

Ndipo sitikukayika.

Khristu adzakwaniritsa

Chifuniro cha Mulungu.

3. Yesu Mfumu, analonjeza

Paradaiso padzikoli.

Tiyamika Atate wathu

Mochokera mumtimamu.

(KOLASI)

Paradaiso adzafika.

Ndipo sitikukayika.

Khristu adzakwaniritsa

Chifuniro cha Mulungu.

(Onaninso Mat. 5:5; 6:10; Yoh. 5:28, 29.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani