LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 24
  • Yang’ananibe Pamphotho!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yang’ananibe Pamphotho!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yang’ana pa Mphoto
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Musalole Ciliconse Kukumanitsani Mphoto
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mtendele Wathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 24

Nyimbo 24

Yang’ananibe Pamphotho!

(2 Akorinto 4:18)

1. Pomwe akhungu adzaona

Ndipo ogontha adzamvanso,

Pamene madzi adzayenda

Ngakhale muchipululu,

Pomwe wolumala ’dzadumpha,

Abale athu sadzafanso,

Mudzaona madalitsowa

M’kayang’anabe pamphotho.

2. Osalankhula ’dzalankhula,

Okalamba ku unyamata,

Pomwe nthaka idzatulutsa

Zinthu zambiri zabwino,

Pomwe ana ’dzaimba nyimbo,

Kudzakhala mtendere konse,

M’dzaona ’kufa atauka,

M’kayang’anabe pamphotho.

3. Mimbulu idzadya ndi nkhosa,

Zilombo zoopsa ndi ng’ombe.

Mwana adzazitsogolera,

Ndipo zidzamvera iye.

Pamene mantha ndi misozi

Zidzakhala zinthu zakale,

Mudzaona zinthu zonsezi,

M’kayang’anabe pamphotho.

(Onaninso Yes. 11:6-9; 35:5-7; Yoh. 11:24.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani