LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 144
  • Yang’ana pa Mphoto

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yang’ana pa Mphoto
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yang’ananibe Pamphotho!
    Imbirani Yehova
  • Musalole Ciliconse Kukumanitsani Mphoto
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 144

NYIMBO 144

Yang’ana pa Mphoto

Yopulinta

(2 Akorinto 4:18)

  1. 1. Osaona adzaonanso.

    Ndipo osamvela ‘dzamvela.

    Ana adzaimba mokondwa.

    Tidzakhala pamtendele.

    Akufa adzaukitsidwa.

    Adzakhala m’dziko labwino.

    (KOLASI)

    Iwe udzaonadi izi—

    Ukayang’ana pamphoto.

  2. 2. Mimbulu na mkango na nkhosa,

    Zidzadya pamodzi na ng’ombe.

    Mwana adzazitsogolela,

    Ndipo zidzamumvelela.

    Zoŵaŵa, misozi na mantha,

    Na kuvutika zidzasila.

    (KOLASI)

    Iwe udzaonadi izi—

    Ukayang’ana pamphoto.

(Onaninso Yes. 11:6-9; 35:5-7; Yoh. 11:24.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani