LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 5
  • Khristu Ndi Chitsanzo Chathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khristu Ndi Chitsanzo Chathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Umoyo wa Mpainiya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Umoyo wa Mpainiya
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Pemphelo la Mtumiki wa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 5

Nyimbo 5

Khristu Ndi Chitsanzo Chathu

(Aroma 5:8)

1. Yehova Mulungu,

Anatikondadi,

Potipatsa Mwana’ke monga dipo.

Khristu anakhala

Mkate woti tidye,

Kuti tipeze moyo wosatha.

2. Khristuyo anati

Tipemphe Mulungu

Kuti dzina lake liyeretsedwe.

Tipemphe Ufumu,

Chifuniro chake,

Ndipo tipemphe chakudya chathu.

3. Cho’nadi cha Yesu

Chinamasula ’nthu

Amene anam’tsata ngati nkhosa.

Tizifesa mbewu

Za Ufumu wake.

Tikatero tipeza chimwemwe.

(Onaninso Mat. 6:9-11; Yoh. 3:16; 6:31-51; Aef. 5:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani