LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 92
  • “Lalikira Mawu”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Lalikira Mawu”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Lalikila Mau”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Uthenga Wabwino Umalalikidwa Motani?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • “Pitani Mukaphunzitse Anthu a Mitundu Yonse Kuti Akhale Ophunzila”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 92

Nyimbo 92

“Lalikira Mawu”

(2 Timoteyo 4:2)

1. Mulungu watilamula,

Ndipo tikufunika kumvera.

Tifotokozeretu anthu

Adziwe chiyembekezo chathu.

(KOLASI)

Lalikira,

Indetu onse amve!

Lalika

Dzikoli lisanathe.

Lalika,

Ofatsa amvetsetse.

Lalika

M’dziko lonse.

2. Mavuto adzatiyesa.

Tingapezeke tikunyozedwa,

N’kulowa m’mavuto a’kulu.

Tidzakhulupirirabe M’lungu.

(KOLASI)

Lalikira,

Indetu onse amve!

Lalika

Dzikoli lisanathe.

Lalika,

Ofatsa amvetsetse.

Lalika

M’dziko lonse.

3. Nthawi ina tidzapeza

Anthu ofunadi kumvetsera.

Tiwaphunzitsa ’pulumuke,

Dzina la Yehova tiyeretse.

(KOLASI)

Lalikira,

Indetu onse amve!

Lalika

Dzikoli lisanathe.

Lalika,

Ofatsa amvetsetse.

Lalika

M’dziko lonse.

(Onaninso Mat. 10:7; 24:14; Mac. 10:42; 1 Pet. 3:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani