LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 102
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Imbani Nafe Nyimbo ya Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
    Imbirani Yehova
  • Yelekeza Uli M’dziko Latsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 102

Nyimbo 102

Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!

(Salimo 98:1)

1. Iyi ndi nyimbo yachisangalalo

Yolemekeza M’lungu wamkulu.

Imatipatsadi chiyembekezo,

Imba nafe nyimbo ya Ufumu.

(KOLASI)

‘Lambirani M’lungu wathu,

Mwana waketu ndi mfumu!

Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu

Tamandani dzina la Mulungu.’

2. Ndi nyimboyi tilengeza Ufumu

Khristu Yesu ndi wolamulira.

Ndipo mtundu watsopano wabadwa

Nawo ukumusangalalira.

(KOLASI)

‘Lambirani M’lungu wathu,

Mwana waketu ndi mfumu!

Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu

Tamandani dzina la Mulungu.’

3. Nyimboyi omwe angaiphunzire

Ndi amene amadzichepetsa.

M’dziko lonse ambiri aphunzira.

Akuitananso anthu ena.

(KOLASI)

‘Lambirani M’lungu wathu,

Mwana waketu ndi mfumu!

Dzaphunzireni nyimbo ya Ufumu

Tamandani dzina la Mulungu.’

(Onaninso Sal. 95:6; 1 Pet. 2:9, 10; Chiv. 12:10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani