LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 74
  • Imbani Nafe Nyimbo ya Ufumu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Imbani Nafe Nyimbo ya Ufumu!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kondani Yehova na Mtima Wanu Wonse
    2019-2020 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 74

NYIMBO 74

Imbani Nafe Nyimbo ya Ufumu!

Yopulinta

(Salimo 98:1)

  1. 1. Nyimbo iyi ni yacisangalalo;

    Imakweza Yehova Mulungu.

    Mau ake amatilimbikitsa.

    Capamodzi bwelani tiimbe.

    (KOLASI)

    ‘Lambilani M’lungu wathu.

    Dziŵitsani anthu onse

    Kuti Yesu ndiye alamulila;

    Tamandani Yehova Mulungu.’

  2. 2. Na nyimboyi tilengeza Ufumu:

    “Khristu Yesu tsopano ni mfumu.”

    Ndipo mtundu watsopano wabadwa;

    Nawo udzalamulila naye.

    (KOLASI)

    ‘Lambilani M’lungu wathu.

    Dziŵitsani anthu onse

    Kuti Yesu ndiye alamulila;

    Tamandani Yehova Mulungu.’

  3. 3. Odzicepetsa angaiphunzile.

    Mau ake ni otsitsimula.

    M’dziko lonse ambili aphunzila,

    Ndipo nawo aitana ena:

    (KOLASI)

    ‘Lambilani M’lungu wathu.

    Dziŵitsani anthu onse

    Kuti Yesu ndiye alamulila;

    Tamandani Yehova Mulungu.’

(Onaninso Sal. 95:6; 1 Pet. 2:9, 10; Chiv. 12:10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani