LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 134
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yelekeza Uli M’dziko Latsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Imbani Nafe Nyimbo ya Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 134

Nyimbo 134

Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

(Chivumbulutso 21:1-5)

1. Yerekeza iwe ndi’ne

M’dziko la tsopano tili tonse.

Ona mmene udzamvere,

Kukhala m’dziko la mtendere.

Oipa onse achoka.

M’lungu wathu sadzalephera

Kusintha zonse padziko lapansi.

Tidzamuimbira nyimbo tikumati:

(KOLASI)

“Yehova M’lungu mwachita bwino,

Zonse zakhalano zatsopano.

Tikuimba nyimbo mwachisangalalo.

Ndinudi woyenera ulemelero.”

2. Taganizira m’tsogolo,

Iwe ndi’ne m’dziko latsopano.

Sitidzamva ndi kuona

Zinthu zotichititsa mantha.

Mmene analonjezera

Zachitika, zonse zatheka.

Tsopano aku’kitsa omwalira,

Iwo ndi ife tidzamuyamikira:

(KOLASI)

“Yehova M’lungu mwachita bwino,

Zonse zakhalano zatsopano.

Tikuimba nyimbo mwachisangalalo.

Ndinudi woyenera ulemelero.”

(Onaninso Sal. 37:10, 11; Yes. 65:17; Yoh. 5:28; 2 Pet. 3:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani