LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 81
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Tiwonjezeleni Cikhulupililo”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
  • “Tionjezeleni Cikhulupililo”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 81

Nyimbo 81

“Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

(Luka 17:5)

1. Yehova nthawi zonse timachimwa

Chifukwa cha kupanda ungwiro.

Pali tchimo lomwe limatikola,

Kusowa kwa chikhulupiriro.

(KOLASI)

M’tiwonjezere chikhulupiriro.

Muzofo’ka zathu m’tithandize.

M’tiwonjezere mwachifundo chanu,

Tikulemekezeni mu zonse.

2. N’zosatheka kukukondweretsani

Ngati sitimakhulupirira.

Chikhulupiriro n’chotiteteza

Ndipo chimatilimbitsa mtima.

(KOLASI)

M’tiwonjezere chikhulupiriro.

Muzofo’ka zathu m’tithandize.

M’tiwonjezere mwachifundo chanu,

Tikulemekezeni mu zonse.

(Onaninso Gen. 8:21; Aheb. 11:6; 12:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani