LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 104
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tamandani Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Ya Kaamba ka Mwana Wake Wodzozedwayo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 104

Nyimbo 103

Tiyeni Tonse Titamande Ya

(Salimo 146:2)

1. Titamande

Ya momveka.

Amatipatsa zonse zabwino.

Titamande

Dzina lake.

Ndi wachikondi, n’ngwamphamvu zonse

Ndipo dzina lake tilengeze.

2. Titamande

Ya chifukwa

Amatimva tikamapemphera.

Dzanja lake

Ndi lamphamvu.

Amalimbikitsa ofooka.

Za mphamvu zake timalengeza.

3. Titamande

Ya mokondwa.

N’ngolungama ndi wodalirika.

Adzakonza

Zolakwika

Ndipo anthu adzadalitsidwa.

Timutamande mosangalala.

(Onaninso Sal. 94:18, 19; 145:21; 147:1; 150:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani