LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 59
  • Tamandani Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Ya Kaamba ka Mwana Wake Wodzozedwayo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tamandani Yehova Chifukwa cha Ufumu Wake
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 59

NYIMBO 59

Tamandani Yehova

Yopulinta

(Salimo 146:2)

  1. 1. Titamande;

    M’lungu wathu.

    Amatipatsa zinthu zabwino.

    Tim’tamande,

    Tim’yamike.

    Iye amakonda anthu onse.

    Conco tilengeze dzina lake.

  2. 2. Titamande;

    M’lungu wathu.

    Amatiyankha tikapemphela.

    Dzanja lake;

    Ndi lamphamvu.

    Amalimbitsa anthu ofo’ka.

    Tilengeze kuti niwamphamvu.

  3. 3. Titamande;

    M’lungu wathu.

    Iye ni wolungama mu zonse.

    Adzakonza;

    Zolakwika.

    Anthu adzapeza madalitso

    Timutamande mosangalala.

(Onaninso Sal. 94:18, 19; 145:21; 147:1; 150:2; Mac. 17:25.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani