LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 61
  • Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mtundu wa Munthu Amene Niyenela Kukhala
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova Alangiza Mwacikondi Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzelu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kutumikila Yehova na Moyo Wonse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yehova Akutipempha Mokoma Mtima Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 61

Nyimbo 61

Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala

(2 Petulo 3:11)

1. Ndithokoze bwanji, ndiperekenji

Kwa inu Yehova chifukwa cha moyo?

Mtima wangawu ndifuna ndiudziwe

Mawu anu Yehova andithandize.

Ndakulonjezani kukhala wanu.

Chifuniro chanu ndichita mwachangu

Ndasankhatu ndekha kutumikira,

Ndisangalatse inu Yehova.

2. Ndithandizenibe kudzifufuza

Ndikhaledi munthu amene mufuna.

Anthu otero mudzawasamalira

Kukhala mmodzi wa iwo ndakhumbira.

(Onaninso Sal. 18:25; 116:12; 119:37; Miy. 11:20.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani