LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 6-7
  • Mawu Oyamba a Cigawo 1

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 1
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Phunzilani Zambili za Yehova Poyang’ana Cilengedwe Cake
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Gwilitsani Nchito Zacilengedwe Pophunzitsa Ana Anu za Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Mmene Cilengedwe Cimaonetsela Cikondi ca Mulungu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Mulungu Anapanga Kumwamba na Dziko Lapansi
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 6-7
Anthu acimwemwe akusangalala na cilengedwe

Mawu Oyamba a Cigawo 1

Baibo imayamba nkhani zake mwa kufotokoza zinthu zokongola zimene Yehova analenga kumwamba na pa dziko lapansi. Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kudziŵa zinthu zodabwitsa za cilengedwe. M’fotokozeleni za mmene Mulungu analengela ise anthu mwapadela kwambili, kupambana nyama. Ife anthu timakamba, kuganiza, kupanga zinthu, kuimba, na kupemphela. M’thandizeni kuyamikila mphamvu za Yehova na nzelu zake, maka-maka cikondi cake pa zinthu zonse zimene analenga—kuphatikizapo aliyense wa ise.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Yehova na Mwana wake anapanga dziko lapansi kuti tikhalepo

  • Yehova anakhazikitsa banja polenga mwamuna na mkazi, na kuwapatsa mphatso yobala ana

  • Colinga ca Yehova n’cakuti anthu akakhale na moyo kwamuyaya, mwa mtendele komanso mogwilizana

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani