LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 38-39
  • Mawu Oyamba a Cigawo 4

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 4
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Mawu Oyamba a Cigawo 11
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • “Woweluza wa Dziko Lonse” Amacita Cilungamo Nthawi Zonse
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mawu Oyamba a Cigawo 5
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Yehova Akukuthandizani Kupambana Mayeso
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 38-39
Mose na Aisiraeli akuona pamene Nyanja Yofiila igaŵika

Mawu Oyamba a Cigawo 4

Cigawo cino cifotokoza za Yosefe, Yobu, Mose, komanso Aisiraeli. Onsewa anavutika kwambili cifukwa ca Mdyelekezi. Ena anacitilidwa zopanda cilungamo, kuponyewa m’ndende, kuikidwa ukapolo, ngakhale kufedwa okondedwa awo mwadzidzidzi. Ngakhale n’telo, Yehova anawateteza m’njila zolekana-lekana. Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kumvetsa mmene atumiki a Yehova anavutikila, koma osataya cikhulupililo cawo.

Yehova anaseŵenzetsa Milili 10 kuonetsa kuti iye ni wamphamvu ngako kupambana milungu yonse ya Aiguputo. Fotokozani mmene Yehova anatetezela anthu ake kumbuyoko, na mmene amawatetezela masiku ano.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Yosefe anakana kucita zaciwelewele cifukwa cokonda Yehova

  • Ngakhale kuti Yobu anavutika kwambili, iye sanasiye Yehova

  • Kulikonse kumene Mose anali, sanaiŵale kuti anali mtumiki wa Mulungu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani