LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 160-161
  • Mawu Oyamba a Cigawo 11

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 11
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Mawu Oyamba a Cigawo 13
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mawu Oyamba a Cigawo 4
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Kodi Yesu Khiristu N’ndani?
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Mawu Oyamba a Cigawo 12
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 160-161
Yosefe aphunzitsa Yesu nchito yaukalipentala, ndipo Mariya ndi abale ena a Yesu ali capafupi

Mawu Oyamba a Cigawo 11

Cigawo cino cifotokoza nkhani za m’Malemba Acigiriki Acikhristu. Yesu anabadwila m’banja yosaukila, imene inali kukhala m’tauni yaing’ono. Anali kuthandiza atate ake pa nchito yawo ya ukalipentala. Yesu ndiye anali kudzapulumutsa mtundu wa anthu. Yehova anam’sankha kukhala Mfumu ya Ufumu wakumwamba. Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kumvetsa kuti Yehova anasankha mosamala banja limene Yesu adzabadwilamo, komanso kumene adzakulila. Fotokozani mmene Yehova anatetezela Yesu kuti asaphedwe na Herode, komanso kuti palibe cingalepheletse colinga ca Yehova. Kambilanani za mmene Yehova anapatsila Yohane nchito yokonzela njila Yesu. Unikani mmene Yesu anaonetsela kuti kuyambila ali mwana, anali kukonda nzelu zocokela kwa Yehova.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Tikhale okhulupilika nthawi zonse ku makonzedwe a Yehova

  • Yesu, Mwana wamphamvu wa Mulungu, analola kudzabadwa pa dziko lapansi monga khanda

  • Yohane M’batizi analengeza za kubwela kwa Mesiya

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani