LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 202-203
  • Mawu Oyamba a Cigawo 13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 13
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Mawu Oyamba a Cigawo 11
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mawu Oyamba a Cigawo 12
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mawu Oyamba a Cigawo 3
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mawu Oyamba a Cigawo 1
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 202-203
Yesu asambika mapazi a atumwi ake

Mawu Oyamba a Cigawo 13

Yesu anabwela pa dziko lapansi kudzapeleka moyo wake kaamba ka anthu opanda ungwilo. Ngakhale anafa, iye anagonjetsa dziko. Yehova anakhulupilika kwa Mwana wake, ndipo anamuukitsa atamwalila. Mpaka imfa yake, Yesu modzicepetsa anali kutumikila ena, ndipo anali kuwakhululukila akalakwitsa. Yesu ataukitsidwa, anaonekelanso kwa ophunzila ake. Anawaphunzitsa mmene angagwilile nchito yofunika kwambili imene anawapatsa. Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kudziŵa kuti, ngakhale masiku ano, tili na mwayi wotengako mbali m’nchito imeneyo.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Kwa Yehova, palibe vuto limene angalephele kulithetsa

  • Khalani na mtima wokonda kutumikila ena na kuwathandiza, monga mmene Yesu anacitila

  • Akhristu oona amadziŵika na cikondi kwa wina na mnzake

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani