LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 174-175
  • Mawu Oyamba a Cigawo 12

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 12
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Coonadi Ponena za Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2020
  • Kodi Tiyenela Kupemphela kwa Yesu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Mawu Oyamba a Cigawo 11
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Kodi Yehova Amamvetsela kwa Ife?
    Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 174-175
Yesu aphunzitsa anthu akulu-akulu komanso ana

Mawu Oyamba a Cigawo 12

Yesu anali kuphunzitsa anthu za Ufumu wa kumwamba. Anaŵaphunzitsanso kuti azipemphela kuti dzina la Mulungu liyeletsedwe, Ufumu wake ubwele, komanso kuti cifunilo cake cicitike pa dziko lapansi. Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kumvetsa kuti pemphelo imeneyi ni yofunika kwambili kwa ise. Yesu sanalole kuti Satana amutaitse cikhulupililo cake mwa Mulungu. Yesu anasankha atumwi ake, oyamba kusankhidwa kuti akalamulile mu Ufumu wa Mulungu. M’cigawo cino, mudzaona kuti Yesu anali wodzipeleka pa kulambila koona. Cinanso, Yesu anali kukonda kuthandiza anthu. N’cifukwa cake anacilitsa odwala, kudyetsa anjala, ngakhalenso kuukitsa akufa. Mwa izi, Yesu anaonetsa zimene Ufumu wa Mulungu udzacitila anthu.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Yesu anapatsa otsatila ake nchito yolalikila za Ufumu wa Mulungu na kupanga ophunzila

  • Popemphela, yambani kupemphelela zokhudza Yehova musanabwele ku zanu

  • Muzikhululuka mocokela pansi pa mtima, ndipo muzicitila ena zimene mungafune kuti akucitileni

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani