LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 58-59
  • Mawu Oyamba a Cigawo 5

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mawu Oyamba a Cigawo 5
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Nkhani Zofanana
  • Mawu Oyamba a Cigawo 11
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Mawu Oyamba a Cigawo 4
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Lonjezo kwa Yehova
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Cihema Colambililako
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Onaninso Zina
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 58-59
Aisiraeli atola mana

Mawu Oyamba a Cigawo 5

Patapita miyezi iŵili, Aisiraeli atawoloka Nyanja Yofiila, anafika pa Phili la Sinai. Pamalo amenewo, Yehova anacita pangano na mtundu wa Isiraeli kuti adzakhala mtundu wake wapadela. Iye anawateteza na kuwapatsa zonse zofunikila monga cakudya ca mana, zovala zimene sizinali kutha, komanso malo okhala otetezeka. Ngati ndimwe kholo, thandizani mwana wanu kumvetsa cifukwa cake Yehova anapatsa Aisiraeli Cilamulo, cihema colambililako, komanso ansembe. Gogomezani kufunika kocita zimene talonjeza, kukhala odzicepetsa, na kukhala okhulupilika kwa Yehova nthawi zonse.

MAPHUNZILO AKULU-AKULU M’CIGAWOCI

  • Ukalonjeza cinthu kwa Yehova, uyenela kucita cimene unalonjeza

  • Kunyada, kudzikonda, na kupanduka kumabweletsa tsoka

  • Yehova anali woleza mtima kwa Aisiraeli, ndipo anali kuwasamalilabe ngakhale pamene anacita zoipa

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani