LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • ca-brpgm17 masa. 1-2
  • Pitilizani Kum’konda Yehova —Mat. 22:37.

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pitilizani Kum’konda Yehova —Mat. 22:37.
  • 2016-2017 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya:
  • Kondani Yehova na Mtima Wanu Wonse
    2019-2020 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Loŵani mu Mpumulo wa Mulungu!
    2023-2024 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Khalani Wolimba!
    Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela wa 2018-2019—Wa Woimila Nthambi
  • Kondwelani Mwa Yehova
    2020-2021 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
Onaninso Zina
2016-2017 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela
ca-brpgm17 masa. 1-2

Msonkhano wa Dela wa Mboni za Yehova

Pulogilamu ya 2016-2017

Mutu: Pitilizani Kum’konda Yehova —Mat. 22:37.

Cigawo ca Kum’mawa

8:40 Nyimbo Zamalimba

8:50 Nyimbo Na. 50 na Pemphelo

9:00 Muzikumbukila Lamulo Lalikulu Kwambili

9:15 Muzikonda Mulungu, Osati Dziko

9:30 Phunzitsani Ena ‘Kukonda Dzina la Yehova’

9:55 Nyimbo Na. 112 na Zilengezo

10:05 “Munthu Amene Amakonda Mulungu Azikondanso M’bale Wake”

10:35 Kudzipeleka na Ubatizo

11:05 Nyimbo Na. 34

Cigawo ca Kumasana

12:20 Nyimbo Zamalimba

12:30 Nyimbo Na. 73

12:35 Zocitika mu Ulaliki

12:45 Cidule ca Nsanja ya Mlonda

13:15 Makolo—Phunzitsani Ana Anu Kukonda Yehova

13:30 Acicepele—Onetsani kuti Yehova Ni Bwenzi Lanu la Pamtima

13:45 Nyimbo Na. 106 na Zilengezo

13:55 Musasiye ‘Cikondi Cimene Munali Naco Poyamba’

14:55 Nyimbo Na. 3 na Pemphelo

Pezani Mayankho pa Mafunso Aya:

1. Kodi lamulo lalikulu ndi liti? Nanga n’cifukwa ciani n’lofunika kwambili? (Mat. 22:​37, 38; Maliko 12:⁠30)

2. Kodi tingapewe bwanji mtima wokonda dziko? (1 Yoh. 2:​15-​17)

3. Kodi tingawaphunzitse bwanji ena ‘kukonda dzina la Yehova’? (Yes. 56:​6, 7)

4. Tingaonetse bwanji cikondi copanda cinyengo kwa abale athu? (1 Yoh. 4:​21)

5. Kodi makolo angaphunzitse bwanji ana awo kukonda Yehova? (Deut. 6:​4-9)

6. Mungaonetse bwanji kuti Yehova ni Bwenzi lanu la pamtima? (1 Yoh. 5:⁠3)

7. Tingacite ciani kuti tipitilize kukonda Yehova, nanga n’ciani cingatithandize kuyambilanso kumukonda ngati cikondico cinazilala? (Chiv. 2:​4, 5)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani