LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • th phunzilo 16 tsa. 19
  • Khalani Wolimbikitsa Komanso Wotsitsimula

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani Wolimbikitsa Komanso Wotsitsimula
  • Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Nkhani Zofanana
  • Yesetsani Kuwafika pa Mtima Omvela
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Kukamba Mwaumoyo
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Kumveketsa Phindu ya Nkhani
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Mzimu Waubwenzi na Cifundo
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
Onaninso Zina
Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
th phunzilo 16 tsa. 19

PHUNZILO 16

Khalani Wolimbikitsa Komanso Wotsitsimula

Lemba losagwila mawu

Yobu 16:5

ZOFUNIKILA: Muzikamba zinthu zothandiza komanso zolimbikitsa.

MOCITILA:

  • Khalani na cidalilo mwa omvela anu. Dalilani kuti iwo ali na mtima wofuna kukondweletsa Yehova. Ngakhale pofuna kupeleka uphungu, coyamba pezani cowayamikila moona mtima.

    Tumalangizo tothandizila

    Mawu anu azicokela mu mtima wacikondi, osati wokhumudwa. Nkhope yomwetulila mwaubwenzi imamasula omvela na kuwalimbikitsa kuchela khutu.

  • Cepetsani kukamba pa zinthu zoipa. Chulani zoipa m’nkhani yanu mongofuna kumveketsa mfundo inayake. Koma mzimu wonse wa nkhani yanu uzikhala pa zinthu zabwino.

  • Seŵenzetsani kwambili Mawu a Mulungu. Unikani zimene Yehova anacita, zimene akucita, na zimene adzacitila anthu. Apatseni ciyembekezo omvela anu na kuwalimbikitsa.

MU ULALIKI

Muziona munthu aliyense kuti akhoza kukhala Mboni.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani